Masalimo 73:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti ndinachitira nsanje odzitamandira, pakuona mtendere wa oipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti ndinachitira nsanje odzitamandira, pakuona mtendere wa oipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pakuti ndinkachita nsanje ndi anthu odzikuza, pamene ndidaona anthu oipa akulemera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pakuti ndinkachitira nsanje odzitamandira, pamene ndinaona mtendere wa anthu oyipa. Onani mutuwo |