Masalimo 73:21 - Buku Lopatulika21 Pakuti mtima wanga udawawa, ndipo ndinalaswa mu impso zanga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pakuti mtima wanga udawawa, ndipo ndinalaswa m'impso zanga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Pamene paja ndinkavutika ndi maganizo, ndi kumamva cholasa mumtimamu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pamene mtima wanga unasautsidwa ndi kuwawidwa mu mzimu mwanga, Onani mutuwo |