Masalimo 73:22 - Buku Lopatulika22 ndinali wam'thengo, wosadziwa kanthu; ndinali ngati nyama pamaso panu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 ndinali wam'thengo, wosadziwa kanthu; ndinali ngati nyama pamaso panu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 ndinali wopusa wosamvetsa kanthu, ndinali ngati chilombo kwa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 ndinali wopusa ndi wosadziwa; ndinali chirombo chopanda nzeru pamaso panu. Onani mutuwo |