Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 73:20 - Buku Lopatulika

20 Monga anthu atauka, apepula loto; momwemo, Inu Ambuye, pakuuka mudzapeputsa chithunzithunzi chao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Monga anthu atauka, apepula loto; momwemo, Inu Ambuye, pakuuka mudzapeputsa chithunzithunzi chao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Inu Ambuye, pamene mudzadzuka mudzaŵanyoza kotheratu, monga momwe munthu amanyozera maloto atadzuka m'maŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Monga loto pamene wina adzuka, kotero pamene Inu muuka, Inu Ambuye, mudzawanyoza ngati maloto chabe.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 73:20
6 Mawu Ofanana  

Adzauluka ngati loto, osapezekanso; nadzaingidwa ngati masomphenya a usiku.


Indedi munthu ayenda ngati mthunzi; Indedi avutika chabe: Asonkhanitsa chuma, ndipo sadziwa adzachilandira ndani?


Ukani Yehova mu mkwiyo wanu, nyamukani chifukwa cha ukali wa akundisautsa; ndipo mugalamukire ine; mwalamulira chiweruzo.


Pamenepo Ambuye anauka ngati wam'tulo; ngati chiphona chakuchita nthungululu ndi vinyo.


Muwatenga ngati ndi madzi aakulu, akhala ngati tulo; mamawa akhala ngati msipu wophuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa