Masalimo 73:16 - Buku Lopatulika16 Pamene ndinayesa kudziwitsa ichi, ndinavutika nacho; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pamene ndinayesa kudziwitsa ichi, ndinavutika nacho; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma pamene ndidalingalira zimenezi kuti ndizimvetse bwino, zidandiwonekera ngati nkhani yovuta, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Pamene ndinayesa kuti ndimvetse zonsezi, zinandisautsa kwambiri Onani mutuwo |