Masalimo 73:15 - Buku Lopatulika15 ndikadati, Ndidzafotokozera chotere, taonani, ndikadachita chosakhulupirika ndi mbadwo wa ana ako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 ndikadati, Ndidzafotokozera chotere, taonani, ndikadachita chosakhulupirika ndi mbadwo wa ana ako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndikadati, “Ndilankhula monga amachitira iwowo,” ndikadakhala wosakhulupirika kwa zidzukulu zanu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndikanati, “Ndidzayankhula motere,” ndikanachita chosakhulupirika kwa ana anu. Onani mutuwo |