Masalimo 73:17 - Buku Lopatulika17 mpaka ndinalowa m'zoyera za Mulungu, ndi kulingalira chitsiriziro chao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 mpaka ndinalowa m'zoyera za Mulungu, ndi kulingalira chitsiriziro chao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 mpaka nditakaloŵa m'malo opatulika a Mulungu, apo mpamene ndidaona mathero ake a anthuwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 kufikira nditalowa mʼmalo opatulika a Mulungu; pamenepo ndinamvetsa mathero awo. Onani mutuwo |