Masalimo 73:14 - Buku Lopatulika14 Popeza andisautsa tsiku lonse, nandilanga mamawa monse, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Popeza andisautsa tsiku lonse, nandilanga mamawa monse, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pakuti ndapeza mavuto tsiku lonse, ndipo ndalangidwa m'maŵa mulimonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Tsiku lonse ndapeza mavuto; ndakhala ndi kulangidwa mmawa uliwonse. Onani mutuwo |