Masalimo 73:13 - Buku Lopatulika13 Indedi, ndinayeretsa mtima wanga kwachabe, ndipo ndinasamba m'manja mosalakwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Indedi, ndinayeretsa mtima wanga kwachabe, ndipo ndinasamba m'manja mosalakwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ine ndasunga mtima wanga woyera, ndasamba m'manja kuwonetsa kuti ndine wosalakwa, koma zonsezi popanda phindu konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndithudi ine ndawusunga pachabe mtima wanga woyera; pachabe ndasamba mʼmanja mwanga mwa kusalakwa kwanga. Onani mutuwo |