Masalimo 72:14 - Buku Lopatulika14 Adzaombola moyo wao ku chinyengo ndi chiwawa; ndipo mwazi wao udzakhala wa mtengo pamaso pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Adzaombola moyo wao ku chinyengo ndi chiwawa; ndipo mwazi wao udzakhala wa mtengo pamaso pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Idzaombola moyo wao kwa anthu oŵapsinja ndi kwa oŵachita zankhanza, pakuti magazi ao ndi amtengowapatali pamaso pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Iye adzalanditsa iwo ku mazunzo ndi chiwawa pakuti magazi awo ndi amtengo wapatali pamaso pake. Onani mutuwo |