Masalimo 71:20 - Buku Lopatulika20 Inu, amene munationetsa nsautso zambiri ndi zoipa, mudzatipatsanso moyo, ndi kutitenganso munsi mwa dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Inu, amene munationetsa nsautso zambiri ndi zoipa, mudzatipatsanso moyo, ndi kutitenganso munsi mwa dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Mudzanditsitsimutsanso Inu amene mwandiwonetsa mavuto ambiri oŵaŵa, mudzanditulutsanso m'dzenje lozama la pansi pa nthaka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ngakhale mwandionetsa mavuto ambiri owawa, mudzabwezeretsanso moyo wanga; kuchokera kunsi kwa dziko lapansi, mudzandiukitsanso. Onani mutuwo |