Masalimo 71:21 - Buku Lopatulika21 Mundionjezere ukulu wanga, ndipo munditembenukire kundisangalatsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Mundionjezere ukulu wanga, ndipo munditembenukire kundisangalatsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Inu mudzaonjezera ulemu wanga ndipo mudzandisangalatsanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Inu mudzachulukitsa ulemu wanga ndi kunditonthozanso. Onani mutuwo |