Masalimo 71:19 - Buku Lopatulika19 Chilungamo chanunso, Mulungu, chifikira kuthambo; Inu amene munachita zazikulu, akunga Inu ndani, Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Chilungamo chanunso, Mulungu, chifikira kuthambo; Inu amene munachita zachikulu, akunga Inu ndani, Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Mphamvu zanu ndi kulungama kwanu, zimafikira mpaka kumwambamwamba. Pali yani wofanafana nanu, Inu Mulungu, amene mwachita zazikulu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mphamvu zanu ndi kulungama kwanu zimafika mpaka kumwambamwamba. Ndani wofanana nanu Inu Mulungu, amene mwachita zazikulu? Onani mutuwo |