Masalimo 71:2 - Buku Lopatulika2 Ndikwatuleni m'chilungamo chanu, ndi kundilanditsa, nditcherereni khutu lanu ndi kundipulumutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndikwatuleni m'chilungamo chanu, ndi kundilanditsa, nditcherereni khutu lanu ndi kundipulumutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Koma mundilanditse ndi kundipulumutsa, pakuti ndinu Mulungu wolungama. Tcherani khutu kuti mundimve, ndipo mundipulumutse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mundilanditse ndi kundipulumutsa mwa chilungamo chanu, mutchere khutu lanu ndi kundipulumutsa. Onani mutuwo |