Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 69:8 - Buku Lopatulika

8 Abale anga andiyesa mlendo, ndi ana a mai wanga andiyesa wa mtundu wina.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Abale anga andiyesa mlendo, ndi ana a mai wanga andiyesa wa mtundu wina.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Kwa abale anga ndasanduka mlendo, kwa ana a mai wanga ndili ngati wakudza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ndine mlendo kwa abale anga, munthu wakudza kwa ana aamuna a amayi anga;

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 69:8
18 Mawu Ofanana  

Ndakhala chotonza chifukwa cha akundisautsa onse, inde, koposa kwa anansi anga; ndipo anzanga andiyesa choopsa; iwo akundipenya pabwalo anandithawa.


Ondikonda ndi anzanga apewa mliri wanga; ndipo anansi anga aima patali.


Chimene adani anu, Yehova, atonza nacho; chimene atonzera nacho mayendedwe a wodzozedwa wanu.


Wodalitsika Yehova kunthawi yonse. Amen ndi Amen.


Ndinapereka msana wanga kwa omenya, ndi masaya anga kwa iwo amene anakudzula tsitsi langa; sindinabisire nkhope yanga manyazi ndi kulavulidwa.


Iye ananyozedwa ndi kukanidwa ndi anthu; munthu wazisoni, ndi wodziwa zowawa; ndipo ananyozedwa monga munthu wombisira anthu nkhope zao; ndipo ife sitinamlemekeze.


Zoonadi Iye ananyamula zowawa zathu, ndi kusenza zisoni zathu; koma ife tinamuyesa wokhomedwa, wokanthidwa ndi Mulungu, ndi wovutidwa.


Inu Yehova, mudziwa; mundikumbukire ine, mundiyang'anire Ine, mundibwezere chilango pa ondisautsa ine; musandichotse m'chipiriro chanu; dziwani kuti chifukwa cha Inu ndanyozedwa.


Koma izi zonse zinachitidwa, kuti zolembedwa za aneneri zikwaniridwe. Pomwepo ophunzira onse anamsiya Iye, nathawa.


Anadza kwa zake za Iye yekha, ndipo ake a mwini yekha sanamlandire Iye.


Pakuti angakhale abale ake sanakhulupirire Iye.


Ndipo Eliabu mkulu wake anamumva iye alikulankhula ndi anthu; ndipo Eliyabu anapsa mtima ndi Davide, nati, Unatsikiranji kuno? Ndi nkhosa zija zowerengeka unazisiya ndi yani, m'chipululu muja? Ine ndidziwa kudzikuza kwako ndi kuipa kwa mtima wako; pakuti watsika kuti udzaone nkhondoyi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa