Masalimo 69:8 - Buku Lopatulika8 Abale anga andiyesa mlendo, ndi ana a mai wanga andiyesa wa mtundu wina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Abale anga andiyesa mlendo, ndi ana a mai wanga andiyesa wa mtundu wina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kwa abale anga ndasanduka mlendo, kwa ana a mai wanga ndili ngati wakudza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndine mlendo kwa abale anga, munthu wakudza kwa ana aamuna a amayi anga; Onani mutuwo |