Masalimo 69:24 - Buku Lopatulika24 Muwatsanulire mkwiyo wanu, ndipo moto wa ukali wanu uwagwere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Muwatsanulire mkwiyo wanu, ndipo moto wa ukali wanu uwagwere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Muŵagwetsere ukali wanu, mkwiyo wanu woyaka moto uŵagwire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Khuthulirani ukali wanu pa iwo; mkwiyo wanu woyaka moto uwathe mphamvu. Onani mutuwo |