Masalimo 69:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo musabisire nkhope yanu mtumiki wanu; pakuti ndisautsika ine; mundiyankhe msanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo musabisire nkhope yanu mtumiki wanu; pakuti ndisautsika ine; mundiyankhe msanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Musandibisire ine mtumiki wanu nkhope yanu, fulumirani kundithandiza, pakuti ndili pa zovuta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Musabisire nkhope yanu mtumiki wanu, ndiyankheni msanga, pakuti ndili pa mavuto. Onani mutuwo |