Masalimo 69:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo ndinalira pa kusala kwa moyo wanga, koma uku kunandikhalira chotonza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo ndinalira pa kusala kwa moyo wanga, koma uku kunandikhalira chotonza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pamene ndidadzilanga posala zakudya, anthu adandinyoza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pamene ndikulira ndi kusala kudya, ndiyenera kupirira kunyozedwa; Onani mutuwo |