Masalimo 68:9 - Buku Lopatulika9 Inu, Mulungu, munavumbitsa chimvula, munatsitsimutsa cholowa chanu pamene chidathodwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Inu, Mulungu, munavumbitsa chimvula, munatsitsimutsa cholowa chanu pamene chidathodwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Inu Mulungu, mudagwetsa mvula yokwanira pa dziko. Mudalimbitsanso dziko, choloŵa cha anthu anu, pamene lidaali lofooka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Munapereka mivumbi yochuluka, Inu Mulungu; munatsitsimutsa cholowa chanu cholefuka. Onani mutuwo |