Masalimo 68:10 - Buku Lopatulika10 Gulu lanu linakhala m'dziko muja. Mwa ukoma wanu munalikonzera ozunzika, Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Gulu lanu linakhala m'dziko muja. Mwa ukoma wanu munalikonzera ozunzika, Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Anthu anu adapezamo malo okhala. Inu Mulungu, mudapatsa anthu osauka zosoŵa zao mwa ubwino wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Anthu anu anakhala mʼmenemo ndipo munapatsa anthu osauka zimene zinkawasowa chifukwa cha ubwino wanu Mulungu. Onani mutuwo |