Masalimo 68:7 - Buku Lopatulika7 Pakutuluka paja, Inu Mulungu, ndi kutsogolera anthu anu, pakuyenda paja Inu m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakutuluka paja, Inu Mulungu, ndi kutsogolera anthu anu, pakuyenda paja Inu m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu Mulungu, pamene munkatsogolera anthu anu, pamene munkayenda m'chipululu muja, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pamene munatuluka kutsogolera anthu anu, Inu Mulungu, pamene munayenda kudutsa chipululu, Onani mutuwo |