Masalimo 68:12 - Buku Lopatulika12 Mafumu a magulu a ankhondo athawathawa, ndipo mkazi amene akhala kwao agawa zofunkha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Mafumu a magulu a ankhondo athawathawa, ndipo mkazi amene akhala kwao agawa zofunkha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Mafumu a magulu a ankhondo akuthaŵa, indedi akuthaŵa. Tsono azimai ku mudzi akugaŵana zofunkha, ngakhale atsalira pakati pa makola ankhosa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Mafumu ndi ankhondo anathawa mwaliwiro; mʼmisasa anthu anagawana zolanda pa nkhondo. Onani mutuwo |