Masalimo 68:13 - Buku Lopatulika13 Pogona inu m'makola a zoweta, mukhala ngati mapiko a njiwa okulira ndi siliva, ndi nthenga zake zokulira ndi golide woyenga wonyezimira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pogona inu m'makola a zoweta, mukhala ngati mapiko a njiwa okulira ndi siliva, ndi nthenga zake zokulira ndi golide woyenga wonyezimira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 “Zofunkhazo zikuwoneka ngati mapiko a nkhunda okutidwa ndi siliva, nthenga zake nzokutidwa ndi golide wonyezemira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ngakhale mukugona pakati pa makola a ziweto, mapiko a nkhunda akutidwa ndi siliva, nthenga zake ndi golide wonyezimira.” Onani mutuwo |