Masalimo 66:19 - Buku Lopatulika19 Koma Mulungu anamvadi; anamvera mau a pemphero langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma Mulungu anamvadi; anamvera mau a pemphero langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Koma zoonadi, Mulungu wandimvera, wasamala mau a pemphero langa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 koma ndithu Mulungu wamvetsera ndipo watchera khutu ku mawu a kupempha kwanga. Onani mutuwo |