Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 66:17 - Buku Lopatulika

17 Ndinamfuulira Iye pakamwa panga, ndipo ndinamkuza ndi lilime langa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndinamfuulira Iye pakamwa panga, ndipo ndinamkuza ndi lilime langa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Ndidafuula kwa Iye, ndipo ndidamtamanda ndi pakamwa panga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ndinafuwula kwa Iye ndi pakamwa panga, matamando ake anali pa lilime panga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 66:17
8 Mawu Ofanana  

Ndidzabwezera Yehova chiyani chifukwa cha zokoma zake zonse anandichitira?


Ndidzakukwezani Mulungu wanga, Mfumu; ndipo ndidzalemekeza dzina lanu kunthawi za nthawi.


Ndidzakukwezani, Yehova; pakuti mwandinyamutsa, ndipo simunandikondwetsere adani anga.


Ndinafuulira kwa Inu, Yehova; kwa Ambuye ndinapemba,


M'mwazi mwanga muli phindu lanji, potsikira ine kudzenje? Ngati fumbi lidzayamika Inu? Ngati lidzalalikira choonadi chanu?


Munthu uyu wozunzika anafuula, ndipo Yehova anamumva, nampulumutsa m'masautso ake onse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa