Masalimo 66:16 - Buku Lopatulika16 Idzani, imvani, inu nonse akuopa Mulungu, ndipo ndidzafotokozera zonse anazichitira moyo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Idzani, imvani, inu nonse akuopa Mulungu, ndipo ndidzafotokozera zonse anazichitira moyo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Bwerani mudzamve, inu nonse amene opembedza Mulungu, ndidzakusimbireni zimene Iye wandichitira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Bwerani ndipo mudzamve inu nonse amene mumaopa Mulungu. Ndidzakuwuzani zimene Iyeyo wandichitira. Onani mutuwo |