Masalimo 65:3 - Buku Lopatulika3 Mphulupulu zinandipambana; koma mudzafafaniza zolakwa zathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mphulupulu zinandilaka; koma mudzafafaniza zolakwa zathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 chifukwa cha machimo ao. Pamene zochimwa zathu zitipambana, Inu mumazifafaniza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamene tinathedwa nzeru ndi machimo, Inu munakhululukira mphulupulu zathu. Onani mutuwo |