Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 60:4 - Buku Lopatulika

4 Koma mwapatsa mbendera akuopa Inu, aikweze chifukwa cha choonadi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Koma mwapatsa mbendera akuopa Inu, aikweze chifukwa cha choonadi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Komabe Inu mwatikwezera mbendera ife amene timakuwopani, kuti tisonkhanireko pothaŵa uta wankhondo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Koma kwa iwo amene amaopa Inu, Inu mwakweza mbendera kuti tisonkhanireko pothawa uta.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 60:4
12 Mawu Ofanana  

Tidzafuula mokondwera mwa chipulumutso chanu, ndipo m'dzina la Mulungu wathu tidzakweza mbendera; Yehova akwaniritse mapempho ako onse.


Ndipo pindulani, mu ukulu wanu yendani, kaamba ka choonadi ndi chifatso ndi chilungamo; ndipo dzanja lanu lidzakuphunzitsani zoopsa.


Ndipo Mose anamanga guwa la nsembe, nalitcha dzina lake Yehova Nisi:


Anandifikitsa kunyumba ya vinyo, mbendera yake yondizolimira inali chikondi.


Ndipo Iye adzaimika mbendera ya amitundu, ndipo adzasonkhanitsa oingitsidwa a Israele, namema obalalika a Yuda, kuchokera kumadera anai a dziko lapansi.


Kwezani mbendera paphiri loti see, kwezani mau kwa iwo, kodolani kuti alowe m'zipata za akulu.


Atero Ambuye Yehova, Taona ndidzakodola anthu a mitundu, ndi kukwezera anthu mbendera yanga; ndipo adzabwera nao ana ako aamuna pa chifuwa chao, ndi ana ako aakazi adzatengedwa pa mapewa ao.


Ndipo Iye adzakwezera a mitundu yakutali mbendera, nadzawaimbira mluzu, achokere ku malekezero a dziko; ndipo taonani, iwo adzadza ndi liwiro msangamsanga;


Chomwecho iwo adzaopa dzina la Yehova kuchokera kumadzulo, ndi ulemerero wake kumene kutulukira dzuwa; pakuti pamene mdani adzafika ngati chigumula, mzimu wa Yehova udzamkwezera mbendera yomletsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa