Masalimo 60:4 - Buku Lopatulika4 Koma mwapatsa mbendera akuopa Inu, aikweze chifukwa cha choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma mwapatsa mbendera akuopa Inu, aikweze chifukwa cha choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Komabe Inu mwatikwezera mbendera ife amene timakuwopani, kuti tisonkhanireko pothaŵa uta wankhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Koma kwa iwo amene amaopa Inu, Inu mwakweza mbendera kuti tisonkhanireko pothawa uta. Onani mutuwo |