Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 59:9 - Buku Lopatulika

9 Inu, mphamvu yanga, ndidzakulindirani; pakuti Mulungu ndiye msanje wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Inu, mphamvu yanga, ndidzakulindirani; pakuti Mulungu ndiye msanje wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Inu mphamvu zanga, maso anga ali pa Inu, pakuti Inu Mulungu ndinu linga langa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Inu mphamvu yanga, ine ndiyangʼana kwa inu; Inu Mulungu, ndinu linga langa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 59:9
18 Mawu Ofanana  

Wokhala m'mwambayo adzaseka; Ambuye adzawanyoza.


Yehova akuvomereze tsiku la nsautso; dzina la Mulungu wa Yakobo likuike pamsanje;


Yehova ndiye kuunika kwanga ndi chipulumutso changa; ndidzaopa yani? Yehova ndiye mphamvu ya moyo wanga; ndidzachita mantha ndi yani?


Yembekeza Yehova, limbika, ndipo Iye adzalimbitsa mtima wako; inde, yembekeza Yehova.


Mulungu ndiye pothawirapo pathu ndi mphamvu yathu, thandizo lopezekeratu m'masautso.


Yehova wa makamu ali ndi ife; Mulungu wa Yakobo ndiye pamsanje pathu.


Ndidzaimbira zakukulemekezani Inu, mphamvu yanga; pakuti Mulungu ndiye msanje wanga, Mulungu wa chifundo changa.


Mulungu ananena kamodzi, ndinachimva kawiri, kuti mphamvu ndi yake ya Mulungu.


Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa; msanje wanga, sindidzagwedezeka kwakukulu.


Ndipo Yehova adzakhala msanje kwa iye wokhalira mphanthi. Msanje m'nyengo za nsautso;


Taonani, Mulungu ndiye chipulumutso changa; ndidzakhulupirira, sindidzaopa; pakuti Yehova Mwini ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga, Iye ndiye chipulumutso changa.


koma iwo amene alindira Yehova adzatenganso mphamvu; adzauluka pamwamba ndi mapiko monga ziombankhanga; adzathamanga koma osalema; adzayenda koma osalefuka.


pomwepo udzakondwa mwa Yehova; ndipo Ine ndidzakuyendetsa pa misanje ya dziko lapansi; ndipo ndidzakudyetsa cholowa cha kholo lako Yakobo; pakuti pakamwa pa Yehova pananenapo.


Yehova, Ambuye, ndiye mphamvu yanga, asanduliza mapazi anga ngati a mbawala, nadzandipondetsa pa misanje yanga.


Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa