Masalimo 59:10 - Buku Lopatulika10 Mulungu wa chifundo changa adzandichingamira, adzandionetsa tsoka la adani anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Mulungu wa chifundo changa adzandichingamira, adzandionetsa tsoka la adani anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mulungu wanga adzandichingamira chifukwa ndi wa chikondi chosasinthika. Mulungu wanga adzandilola kuti ndisangalale poona adani anga atagonja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mulungu wanga wachikondi. Mulungu adzapita patsogolo panga ndipo adzandilola kunyada pa iwo amene amandinyoza. Onani mutuwo |