Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 59:7 - Buku Lopatulika

7 Onani abwetuka pakamwa pao; m'milomo mwao muli lupanga, pakuti amati, Amva ndani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Onani abwetuka pakamwa pao; m'milomo mwao muli lupanga, pakuti amati, Amva ndani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Awo ali ukowo, akulongolola kwambiri, ndipo akufuula mwankhalwe, chifukwa m'maganizo mwao amati, “Ndani akutimva nanga?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Onani zomwe amalavula mʼkamwa mwawo; iwo amalavula malupanga kuchokera pa milomo yawo, ndipo amanena kuti, “Ndani angatimve?”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 59:7
16 Mawu Ofanana  

Anena m'mtima mwake, Mulungu waiwala; wabisa nkhope yake; sapenya nthawi zonse.


Woipa anyozeranji Mulungu, anena m'mtima mwake, Simudzafunsira?


Pakamwa pake mposalala ngati mafuta amkaka, koma mumtima mwake munali nkhondo, mau ake ngofewa ngati mafuta oyenga, koma anali malupanga osololasolola.


Moyo wanga uli pakati pa mikango; ndigona pakati pa oyaka moto, ndiwo ana a anthu amene mano ao ali nthungo ndi mivi, ndipo lilime lao ndilo lupanga lakuthwa.


Namati, Akachidziwa bwanji Mulungu? Kodi Wam'mwambamwamba ali nayo nzeru?


Anena mau, alankhula zowawa; adzitamandira onse ochita zopanda pake.


Alipo wonena mwansontho ngati kupyoza kwa lupanga; koma lilime la anzeru lilamitsa.


Lilime la anzeru linena bwino zomwe adziwa; koma m'kamwa mwa opusa mutsanulira utsiru.


Mtima wa wolungama uganizira za mayankhidwe; koma m'kamwa mwa ochimwa mutsanulira zoipa.


Kodi sulingalira chomwe anena anthu awa, kuti, Mabanja awiri amene Yehova anawasankha, wataya iwo? Chomwecho anyoza anthu anga, kuti asakhalenso mtundu pamaso pao.


milomo ya akutsutsana nane ndi zolingalira zao za pa ine tsiku lonse.


Akubadwa inu a njoka, mungathe bwanji kulankhula zabwino, inu akukhala oipa? Pakuti m'kamwa mungolankhula mwa kusefuka kwake kwa mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa