Masalimo 59:4 - Buku Lopatulika4 osawapatsa chifukwa ine, athamanga nadzikonza. Galamukani kukomana nane, ndipo penyani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 osawapatsa chifukwa ine, athamanga nadzikonza. Galamukani kukomana nane, ndipo penyani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 ngakhale sindidalakwe, anthuwo akuthamanga kukonzekera nkhondo. Dzambatukani, mudzandithandize, ndipo muwone. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ine sindinachite cholakwa, koma iwo ndi okonzeka kundithira nkhondo. Dzukani kuti mundithandize; penyani mavuto anga! Onani mutuwo |