Masalimo 59:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti onani, alalira moyo wanga; amphamvu andipangira chiwembu, osachimwa, osalakwa ine, Yehova, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti onani, alalira moyo wanga; amphamvu andipangira chiwembu, osachimwa, osalakwa ine, Yehova, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Onani, iwo akubisalira moyo wanga, anthu oopsa agwirizana kuti andithire nkhondo. Ngakhale sindidachite choipa kapena kuchimwa konse, Inu Chauta, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Onani momwe iwo akundibisalira! Anthu owopsa agwirizana zolimbana nane; osati chifukwa cha mlandu kapena tchimo langa, Inu Yehova. Onani mutuwo |