Masalimo 58:3 - Buku Lopatulika3 Oipa achita chilendo chibadwire, asokera kuyambira kubadwa kwao, nanena bodza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Oipa achita chilendo chibadwire, asokera kuyambira kubadwa kwao, nanena bodza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Anthu oipa ndi osokera kuyambira ali m'mimba mwa mai ao, anthu amabodza ndi otayika kuyambira tsiku la kubadwa kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ngakhale kuchokera tsiku lawo lobadwa oyipa amasochera; kuchokera mʼmimba ya amayi awo, iwo ndi otayika ndipo amayankhula mabodza. Onani mutuwo |