Masalimo 58:4 - Buku Lopatulika4 Ululu wao ukunga wa njoka; akunga mphiri yogontha m'khutu, itseka m'khutu mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ululu wao ukunga wa njoka; akunga mphiri yogontha m'khutu, itseka m'khutu mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ali ndi ululu wonga wa njoka, ali ngati mphiri yogontha, imene yatseka makutu ake, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ululu wawo uli ngati ululu wa njoka, ngati uja wa mphiri imene yatseka mʼmakutu mwake. Onani mutuwo |