Masalimo 58:2 - Buku Lopatulika2 Inde, mumtima muchita zosalungama; padziko lapansi mugawira anthu chiwawa cha m'manja mwanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Inde, mumtima muchita zosalungama; pa dziko lapansi mugawira anthu chiwawa cha m'manja mwanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iyai, mitima yanu imangolingalira zoipa, kuweruza kwanu kosalungama kumadzetsa chiwawa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ayi, mʼmitima mwanu mumakonzekera zosalungama, ndipo manja anu amatulutsa zachiwawa pa dziko lapansi. Onani mutuwo |