Masalimo 56:9 - Buku Lopatulika9 Pamenepo adani anga adzabwerera m'mbuyo tsiku lakuitana ine. Ichi ndidziwa, kuti Mulungu avomerezana nane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pamenepo adani anga adzabwerera m'mbuyo tsiku lakuitana ine. Ichi ndidziwa, kuti Mulungu avomerezana nane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono adani anga adzabwezedwa m'mbuyo pa tsiku lomwe ndidzaitana Mulungu. Ndikudziŵa kuti Mulungu ali pa mbali yanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Adani anga adzabwerera mʼmbuyo pamene ndidzalirira kwa Inu. Pamenepo ndidzadziwa kuti Mulungu ali ku mbali yanga. Onani mutuwo |