Masalimo 56:8 - Buku Lopatulika8 Muwerenga kuthawathawa kwanga, sungani misozi yanga m'nsupa yanu; kodi siikhala m'buku mwanu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Muwerenga kuthawathawa kwanga, sungani misozi yanga m'nsupa yanu; kodi siikhala m'buku mwanu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inu mwaona kupiripita kwanga, mudziŵa kuchuluka kwa misozi yanga. Kodi zonsezi sizidalembedwe m'buku lanu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mulembe za kulira kwanga, mulembe chiwerengero cha misozi yanga mʼbuku lanu. Kodi zimenezi sizinalembedwe mʼbuku lanulo? Onani mutuwo |