Masalimo 56:10 - Buku Lopatulika10 Mwa Mulungu ndidzalemekeza mau ake, mwa Yehova ndidzalemekeza mau ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Mwa Mulungu ndidzalemekeza mau ake, mwa Yehova ndidzalemekeza mau ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndimatamanda Mulungu chifukwa cha mau ake. Ndimatamanda Chauta chifukwa cha zimene wandilonjeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mwa Mulungu amene mawu ake ndimawatamanda, mwa Yehova amene mawu ake ndimawatamanda, Onani mutuwo |