Masalimo 56:4 - Buku Lopatulika4 Mwa Mulungu ndidzalemekeza mau ake, ndakhulupirira Mulungu, sindidzaopa; anthu adzandichitanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mwa Mulungu ndidzalemekeza mau ake, ndakhulupirira Mulungu, sindidzaopa; anthu adzandichitanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndimatamanda Mulungu chifukwa cha zimene wandilonjeza. Ndimakhulupirira Mulungu mopanda mantha. Kodi munthu angandichite chiyani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mwa Mulungu, amene mawu ake ine ndimatamanda, mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha. Kodi munthu amene amafa angandichite chiyani? Onani mutuwo |