Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 56:3 - Buku Lopatulika

3 Tsiku lakuopa ine, ndidzakhulupirira Inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Tsiku lakuopa ine, ndidzakhulupirira Inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Pamene ndichita mantha ndimadalira Inu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ndikachita mantha ndimadalira Inu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 56:3
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehosafati anachita mantha, nalunjikitsa nkhope yake kufuna Yehova, nalalikira kusala mwa Ayuda onse.


Ndakhulupirira Yehova, mutani nkunena kwa moyo wanga, Thawirani kuphiri lanu ngati mbalame?


Ndinafuna Yehova ndipo anandivomera, nandilanditsa m'mantha anga onse.


Ndipo Davide ananyamuka, nathawa tsiku lomwelo chifukwa cha kuopa Saulo, namuka kwa Akisi mfumu ya ku Gati.


Ndipo Davide anasunga mau awa mumtima mwake, naopa kwambiri Akisi mfumu ya Gati.


Ndipo Davide anadololoka kwambiri, pakuti anthu ananena za kumponya iye miyala, pakuti mtima wao wa anthu onse unali ndi chisoni, yense chifukwa cha ana ake aamuna ndi aakazi. Koma Davide anadzilimbikitsa mwa Yehova Mulungu wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa