Masalimo 56:5 - Buku Lopatulika5 Tsiku lonse atenderuza mau anga, zolingirira zao zonse zili pa ine kundichitira choipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Tsiku lonse atenderuza mau anga, zolingirira zao zonse zili pa ine kundichitira choipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsiku lonse adaniwo amafunafuna kulepheretsa zolinga zanga. Zonse zimene amaganiza ndi zoti andichite zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Tsiku lonse amatembenuza mawu anga; nthawi zonse amakonza zondivulaza. Onani mutuwo |