Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 56:5 - Buku Lopatulika

5 Tsiku lonse atenderuza mau anga, zolingirira zao zonse zili pa ine kundichitira choipa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Tsiku lonse atenderuza mau anga, zolingirira zao zonse zili pa ine kundichitira choipa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Tsiku lonse adaniwo amafunafuna kulepheretsa zolinga zanga. Zonse zimene amaganiza ndi zoti andichite zoipa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Tsiku lonse amatembenuza mawu anga; nthawi zonse amakonza zondivulaza.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 56:5
17 Mawu Ofanana  

Ndipo Eliya ananka kukadzionetsa kwa Ahabu. Ndipo njala inali yaikulu mu Samariya.


Yehova ndi wanga; sindidzaopa; adzandichitanji munthu?


Onse akudana nane andinong'onezerana; apangana chondiipsa ine.


Iwo akutama kulemera kwao; nadzitamandira pa kuchuluka kwa chuma chao;


Ndipo iwo anati, Tiyeni, tilingalire Yeremiya chomchitira choipa; pakuti chilamulo sichidzathera wansembe, kapena uphungu wanzeru, kapena mau mneneri. Tiyeni, timpande iye ndi lilime, tisamvere iye mau ake ali onse.


Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwake.


nati, Uyu ananena kuti, Ndikhoza kupasula Kachisi wa Mulunguyu, ndi kummanganso masiku atatu.


namlindira akakole kanthu kotuluka m'kamwa mwake.


Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.


monganso m'makalata ake onse pokamba momwemo za izi; m'menemo muli zina zovuta kuzizindikira, zimene anthu osaphunzira ndi osakhazikika apotoza, monganso atero nao malembo ena, ndi kudziononga nao eni.


Ndipo Saulo anati kwa Davide, Ona, mwana wanga wamkazi wamkulu, dzina lake Merabi, iyeyo ndidzakupatsa akhale mkazi wako; koma undikhalire ngwazi, nuponye nkhondo za Yehova. Pakuti Saulo anati, Dzanja langa lisamkhudze, koma dzanja la Afilisti ndilo.


Nati Saulo, Ndidzampatsa iye, kuti amkhalire msampha, ndi kuti dzanja la Afilisti limgwere. Chifukwa chake Saulo ananena ndi Davide, Lero udzakhala mkamwini wanga kachiwiri.


Saulo nayamba kumuopa Davide kopambana; ndi Saulo anali mdani wa Davide masiku onse.


Ndipo Saulo anamponyera mkondo kuti amgwaze; momwemo Yonatani anazindikira kuti atate wake anatsimikiza mtima kupha Davide.


Tsono akati, Chabwino; kapolo wako adzakhala ndi mtendere; koma akapsa mtima, uzindikirepo kuti anatsimikiza mtima kundichitira choipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa