Masalimo 55:7 - Buku Lopatulika7 Onani, ndikadathawira kutali, ndikadagona m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Onani, ndikadathawira kutali, ndikadagona m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inde, ndikadathaŵira kutali ndi kukakhala ku chipululu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndikanathawira kutali ndi kukakhala mʼchipululu. Onani mutuwo |