Masalimo 55:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo ndinati, Ha, wina akadandipatsa mapiko onga a njiwa! Mwenzi nditauluka, ndi kukhaliratu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo ndinati, Ha, wina akadandipatsa mapiko onga a njiwa! Mwenzi nditauluka, ndi kukhaliratu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo ndimati, “Ndikadakhala ndi mapiko onga a njiŵa, bwenzi nditauluka kupita kutali kukapuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndinati, “Ndithu, ndikanakhala ndi mapiko ankhunda! Ndikanawulukira kutali ndi kukapuma. Onani mutuwo |