Masalimo 55:4 - Buku Lopatulika4 Mtima wanga uwawa m'kati mwanga; ndipo zoopsa za imfa zandigwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mtima wanga uwawa m'kati mwanga; ndipo zoopsa za imfa zandigwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mtima wanga ukumva ululu woopsa, zoopsa za imfa zandigwera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mtima wanga ukupweteka mʼkati mwanga; mantha a imfa andigwera. Onani mutuwo |