Masalimo 55:2 - Buku Lopatulika2 Mverani, ndipo mundiyankhe, ndiliralira m'kudandaula kwanga ndi kubuula; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mverani, ndipo mundiyankhe, ndiliralira m'kudandaula kwanga ndi kubuula; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mundimvere, ndipo mundiyankhe. Mtima wanga suli m'malo chifukwa cha mavuto anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 mverani ndipo mundiyankhe. Maganizo anga akundisautsa ndipo ndathedwa nzeru Onani mutuwo |