Masalimo 53:2 - Buku Lopatulika2 Mulungu m'mwamba anaweramira pa ana a anthu, kuti aone ngati aliko wanzeru, wakufuna Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mulungu m'mwamba anaweramira pa ana a anthu, kuti aone ngati aliko wanzeru, wakufuna Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mulungu kumwambako waŵerama, akuyang'ana anthu pansi pano, kuti aone ngati angakhalepo mmodzi wanzeru wofunitsitsa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mulungu kumwamba amayangʼana pansi pano pa ana a anthu kuti aone ngati alipo wina wanzeru, wofunafuna Mulungu. Onani mutuwo |