Masalimo 52:7 - Buku Lopatulika7 Tapenyani, suyu munthuyu amene sanamuyese Mulungu mphamvu yake; amene anatama kuchuluka kwa chuma chake, nadzilimbitsa m'kuipsa kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Tapenyani, suyu munthuyu amene sanamuyese Mulungu mphamvu yake; amene anatama kuchuluka kwa chuma chake, nadzilimbitsa m'kuipsa kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Muwoneni munthu amene sadafune kudalira Mulungu, koma adakhulupirira chuma chake chochuluka, nalimbikira kuchita zoipa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Pano tsopano pali munthu amene sanayese Mulungu linga lake, koma anakhulupirira chuma chake chambiri nalimbika kuchita zoyipa!” Onani mutuwo |