Masalimo 51:5 - Buku Lopatulika5 Onani, ndinabadwa m'mphulupulu, ndipo mai wanga anandilandira m'zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Onani, ndinabadwa m'mphulupulu, ndipo mai wanga anandilandira m'zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Zoonadi, ndidabadwa mu uchimo, ndinali mu uchimo kuyambira pamene mai wanga adatenga pathupi pa ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa, wochimwa kuyambira pa nthawi imene amayi anga anakhala woyembekezera ine. Onani mutuwo |