Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 50:9 - Buku Lopatulika

9 Sindidzatenga ng'ombe m'nyumba mwako, kapena mbuzi m'makola mwako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Sindidzatenga ng'ombe m'nyumba mwako, kapena mbuzi m'makola mwako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Ndithudi, sindilandira ng'ombe kapena mbuzi iliyonse ya m'makola anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ine sindikufuna ngʼombe yayimuna kuchokera mʼkhola lako kapena mbuzi za mʼkhola lako,

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 50:9
6 Mawu Ofanana  

Pamenepo ndinati, Taonani, ndadza; m'buku mwalembedwa za Ine,


Ndipo chidzakomera Yehova koposa ng'ombe, inde mphongo za nyanga ndi ziboda.


satumikiridwa ndi manja a anthu, monga wosowa kanthu, popeza Iye mwini apatsa zonse moyo ndi mpweya ndi zinthu zonse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa